Search lyrics

Typing something do you want to search. Exam: Artist, Song, Album,Writer, Release Year...
if you want to find exactly, Please input keywords with double-quote or using multi keywords. Exam: "Keyword 1" "Keyword 2"

National Anthem

Malawi Native Anthem Text Lyrics - National Anthem

1. 

Mlungu dalitsani Malawi, 

Mumsunge m'mtendere. 

Gonjetsani adani onse, 

Njala, nthenda, nsanje. 

Lunzitsani mitima yathu, 

Kuti tisaope. 

Mdalitse Mtsogo leri na fe, 

Ndi Mai Malawi. 

2. 

Malawi ndziko lokongola, 

La chonde ndi ufulu, 

Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri, 

Ndithudi tadala. 

Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu, 

N'mphatso zaulere. 

Nkhalango, madambo abwino. 

Ngwokoma Malawi. 

3. 

O! Ufulu tigwirizane, 

Kukweza Malawi. 

Ndi chikondi, khama, kumvera, 

Timutumikire. 

Pa nkhondo nkana pa mtendere, 

Cholinga n'chimodzi. 

Mai, bambo, tidzipereke, 

Pokweza Malawi. 

Sent by Carlos Andr Pereira da Silva Branco 

Copyright: Song Discussions Is Protected By U.s. Patent 9401941. Other Patents Pending.